14/07/2025
#
Ilyas Abdul Karim, phungu wadera la kumwera kwa boma la Chikwawa waulura kuti ayima payekha pachisankho chikudzachi.
Iye anali wa chipani cha Malawi Congress MCP.
Ndipo waulura izi lero pa Ngabu pomwe Pali mafumu ndi anthu osiyananasiyana